lucius banda – chiyanjano lyrics
[chorus]
oooh chiyanjano, chiyanjano
ndicha ntundu wanji?
oooh chiyanjano, chiyanjano
ch-nkandidabwitsa
[verse 1]
chiyanjano chanu chonde amalume
ndi gulu lanu ch-nkandidabwitsa
ufumu wanji wapa chiweniweni
nd-nkadziwa izi sizidzatha bwino
ubwezi wanji wosa dzuzulana
tikudana, tikutha anthu athu
jakisoni ochiritsa anthu
ndiyemweyo inu munkaphera anthu oh!
[chorus x2]
[verse 2]
lero muku[?] taganizani ndalama ndi za chani izi?
mano akatha musamaswe phale
mulekere wana apitilize kukazinga
chifundo chake chiribe malire
muk-mbukire mbala pa ntanda paja
ndalama mwabisazi mukanapatsa amphawi
mukanagula ufumu wa k-mwamba oh!
[chorus x2]
[verse 3]
malume zinthu zikamangoyenda bwino
zikavuta, zikavuta zimavutiratu
malume maudindo anachulukitsa
nd-nkadziwa mudzathera m’ndende
azakhali nawo kuuma ntima
munthu wa mayi koma m’maso muli gwa!
ndalama mwabisazi mukanapatsa amphawi
mukanagula ufumu wa k-mwamba oh!
[chorus x2]
[chorus x4]
Random Lyrics
- alexfroot – odessa lyrics
- samara – ala3bi lyrics
- billy milligan – вверх-вниз (up down) lyrics
- el momo y jona – no more drama lyrics
- tankcsapda – kicsikét lyrics
- eugénie – sur la mer lyrics
- traider – neidische blicke lyrics
- ozel – bonita lyrics
- nathan asher and the infantry – the flag is waving you lyrics
- comaniac – secret seed lyrics