lulu & mathumela band – ndileke lyrics
[verse 1]
pomwe ndikufunitsitsa ndipamene wandisiya
ulibe nazo ntchito olo ntagwera mutu
suk+mva za munthu
koma ine wandisiya ndi ludzu
ndimafunabe pang’ono
pang’ono nk+makuphuzira
[refrain]
darlie tulo [?]
wandikhapila kosathwa
komano ndayesetsa ndafika potopa
ati sudzasiya kundikonda, k+mawuza anthu ena
tsono ngati umandikonda bwanji suli ndine?
tsono taleka ndikuwuze
[pre+chorus]
ndinakupilira mu nzinthu zambiri
zina zoyipa ndimamva titasiyana
koma ukati ulile bodza
uwonetsa kankhope ka m’ngelo
anzako ena ankandifunsiraso
ndilibe chipongwe chabe nd+nkakana
koma ukati undiyalutse anzako akuwona
[chorus]
basi
oh, basi ndileke
basi
oh, basi ndileke
[verse 2]
ngakhale pandekha osandilankhula (no)
ukakhalakhala osafusa za ine (no)
ukamagona usalote ine
(enough is enough, ine ndatopa)
unandichotsa mtima kuyika mwala
pano onse ondiwuza amandikonda
nkaw+ng’ana ndikulira
unandichotsera umunthu w+nga
tsiku osatha ndilire, ndilire, ndilire
[refrain]
ati sudzasiya kundikonda, k+mawuza anthu ena
tsono ngati umandikonda bwanji suli ndine?
tsono taleka ndikuwuze
[pre+chorus]
ndinakupilira mu nzinthu zambiri
zina zoyipa ndimamva titasiyana
koma ukati ulile bodza
uwonetsa kankhope ka m’ngelo
anzako ena ankandifunsiraso
ndilibe chipongwe chabe nd+nkakana
koma ukati undiyalutse anzako akuwona
[chorus]
basi
oh, basi ndileke
basi
oh, basi ndileke
basi
oh, basi ndileke
basi
oh, basi ndileke
Random Lyrics
- jazzy vee – live it up lyrics
- muddasheep – sleeping sheep lyrics
- jswagz tg – ijo lyrics
- rain bisou – new supply lyrics
- kennedy cole – what’s the scouts lyrics
- chael blinya – house party too long lyrics
- rosalie finther – game over lyrics
- boo-ker blahzay – you don’t love me lyrics
- mai huy thắng – chầm chậm chút thôi lyrics
- the ninth hour musical – prologue lyrics