national anthem – malawi native anthem text lyrics
Loading...
1.
mlungu dalitsani malawi,
mumsunge m’mtendere.
gonjetsani adani onse,
njala, nthenda, nsanje.
lunzitsani mitima yathu,
kuti tisaope.
mdalitse mtsogo leri na fe,
ndi mai malawi.
2.
malawi ndziko lokongola,
la chonde ndi ufulu,
nyanja ndi mphepo ya m’mapiri,
ndithudi tadala.
zigwa, mapiri, nthaka, dzinthu,
n’mphatso zaulere.
nkhalango, madambo abwino.
ngwokoma malawi.
3.
o! ufulu tigwirizane,
kukweza malawi.
ndi chikondi, khama, k-mvera,
timutumikire.
pa nkhondo nkana pa mtendere,
cholinga n’chimodzi.
mai, bambo, tidzipereke,
pokweza malawi.
sent by carlos andré pereira da silva branco
Random Lyrics
- pedro the lion – beauty queens lyrics
- save the last dance – murder she wrote lyrics
- pedro the lion – breadwinner you lyrics
- pedro the lion – discretion lyrics
- pedro the lion – diamond ring lyrics
- save the last dance – only you ( bad boy remix) lyrics
- save the last dance – u know whats up lyrics
- nat king cole – funny lyrics
- nat king cole – don’t blame me lyrics
- save the last dance – you can do it lyrics